Mawu a M'munsi
b Anthufe timalakalaka kuchita zoipa chifukwa tinatengera uchimo kwa kholo lathu Adamu. Iye limodzi ndi mkazi wake Hava, anachimwira Mulungu n’kutaya mwayi wokhala ndi moyo wangwiro ndipo zimenezi zinakhudzanso mbadwa zawo zonse.—Genesis 3:17-19; Aroma 5:12.