Mawu a M'munsi
a Yesu “sanachite tchimo.” (1 Petulo 2:21, 22) Choncho sanabatizidwe chifukwa choti ankafunika kulapa machimo koma chifukwa chosonyeza kuti wadzipereka kwa Mulungu kuti achite zofuna zake. Izi zinaphatikizapo kupereka moyo wake chifukwa cha ife.—Aheberi 10:7-10.