Mawu a M'munsi
b Baibulo la King James, limamaliza Pemphero la Ambuye ndi mawu akuti: ‘Kwa inu kukhale ufumu, ndi mphamvu, ndiponso ulemerero mpaka muyaya. Ame.’ Mawu amenewa amapezekanso m’Mabaibulo ena. Komabe, buku lina lofotokoza mawu a m’Baibulo linanena kuti: ‘Mawu amenewa . . . . sapezeka m’mipukutu yodalirika yakale ya Baibulo.’—The Jerome Biblical Commentary.