Mawu a M'munsi
a Buku lina lomwe analemba E. W. Barnes limati: “Tikaona bwinobwino maumboni amene alipo, amasonyeza kuti pofika m’nthawi ya Marcus Aurelius [yemwe anali Mfumu yachiroma kuyambira mu 161 kudzafika mu 180 C.E.] palibe Mkhristu amene analowa usilikali; komanso palibe amene anapitiriza kugwira ntchito yausilikali atakhala Mkhristu.”—The Rise of Christianity.