Mawu a M'munsi
a M’Bungwe la Zipembedzo za ku Ukraine (UCCRO), muli zipembedzo zokwanira 15. Zina mwa zipembedzozi ndi monga Orthodox, Akatolika a Chiroma ndi Chigiriki, Apulotesitanti, magulu atchalitchi cha Evangelical, Ayuda komanso Asilamu.
a M’Bungwe la Zipembedzo za ku Ukraine (UCCRO), muli zipembedzo zokwanira 15. Zina mwa zipembedzozi ndi monga Orthodox, Akatolika a Chiroma ndi Chigiriki, Apulotesitanti, magulu atchalitchi cha Evangelical, Ayuda komanso Asilamu.