Mawu a M'munsi
a “Nzeru zopangidwa ndi anthu” (Artificial intelligence kapena kuti “AI”) zikutanthauza makompyuta kapena makina oyendetsedwa ndi makompyuta, manetiweki kapenanso luso la zipangizo zamakono zomwe zimakonzedwa m’njira yoti zizitha kuphunzira kapena kutengera mmene anthu amaganizira komanso kuchitira zinthu.