Mawu a M'munsi
b Akulu ndi amuna okhulupirika komanso odziwa zambiri amene amaphunzitsa mfundo za m’Malemba komanso kuweta anthu a Yehova powathandiza ndiponso kuwalimbikitsa. Akuluwa akamagwira ntchito imeneyi salandira malipiro aliwonse.—1 Petulo 5:1-3.