Mawu a M'munsi
c Zikafika poipa kwambiri, munthu angathe kuchoka mumpingo komanso kumachita zinthu zomwe zingasokoneze mpingowo ndi kufooketsa Akhristu, kapena angamalimbikitse ena kuti azichita zinthu zoipa. Zimenezi zikachitika, timatsatira lamulo la m’Baibulo lakuti tipewe “kumupatsa moni” munthu wotereyu.—2 Yohane 9-11.