Mawu a M'munsi
a Mwachitsanzo, buku lakuti Encyclopædia Britannica limanena kuti manda otchedwa Taj Mahal anamangidwa ndi Shah Jahān yemwe anali mfumu ya ku Mughal. Komatu sikuti iyeyo ndi amene anamangadi chifukwa nkhaniyo imapitiriza kuti “anthu oposa 20,000 analembedwa ntchito kuti amange mandawo.”