Mawu a M'munsi
a Anthu ena anganene kuti anthu ndi anzeru chifukwa chakuti ali ndi ubongo waukulu kuposa ubongo wa anyani. Mungapeze zifukwa zokuthandizani kuona kuti maganizo amenewa ndi olakwika, m’kabuku kachingelezi kakuti, The Origin of Life—Five Questions Worth Asking, tsamba 28.