Mawu a M'munsi
b Buku lina linati: “Nthawi ina Ukapolo utatha anthu anayamba kulemekeza kwambiri dzina lakuti Yahweh ndipo ankaopa kulitchula, m’malomwake anayamba kugwiritsa ntchito mawu akuti ADONAI kapena ELOHIM m’malo onse amene linkapezeka.”—The New Catholic Encyclopedia, Second Edition, Volume 14, tsamba 883-884