Mawu a M'munsi
b M’malembawa, Mabaibulo ena amagwiritsa ntchito mawu akuti “mthandizi,” “mtsogoleri” kapena “munthu” chabe m’malo monena kuti “mpulumutsi.” Koma mawu achiheberi oyambirira omwe anagwiritsidwa ntchito m’malembawa ndi ofanana ndi mawu amene amagwiritsidwa ntchito ponena kuti Yehova Mulungu ndi Mpulumutsi.—Salimo 7:10.