Mawu a M'munsi
d Onani buku lakuti, Vine’s Complete Expository Dictionary of Old and New Testament Words. Mawu achigiriki omwe anamasuliridwa kuti “onse” ndi ofanana ndi amene anamasuliridwa kuti “zamtundu uliwonse” palemba la Mateyu 5:11. Palembali Yesu anauza otsatira ake kuti anthu adzakunenerani “zoipa zamtundu uliwonse.”—Baibulo la International Standard Version.