Mawu a M'munsi
g Baibulo limagwiritsa ntchito mawu akuti “maubatizo” pofotokoza miyambo inayake yoyeretsa zinthu, monga kuthira madzi pa ziwiya. (Maliko 7:4; Aheberi 9:10) Zimenezi n’zosiyana ndi ubatizo wa Yesu ndi otsatira ake woviika thupi lonse m’madzi.