Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Anthu a ku Babulo ndi amene anayambitsa chikhulupiriro chakuti munthu akamwalira mzimu wake umapitirizabe kukhala ndi moyo, komanso chakuti munthu akafa amakabadwanso kwinakwake. Kenako, akatswiri a nzeru za anthu a ku India anayambitsa chiphunzitso chotchedwa Karma. Buku lina linanena kuti Karma ndi “lamulo lomwe limanena kuti zimene munthu akuchita m’moyo uno, zimadzakhala ndi zotsatira zake m’moyo wotsatira.”​—Britannica Encyclopedia of World Religions, tsamba  913.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena