Mawu a M'munsi
a Sikuti machimo otchulidwa pa Agalatiya 5:19-21 ndi okhawa omwe ndi akuluakulu, chifukwa pambuyo potchula machimo amenewa, Baibulo limanenanso kuti “ndi zina zotero.” Izi zikutanthauza kuti aliyense ayenera kugwiritsa ntchito luso la kuzindikira kuti apeze makhalidwe enanso oipa omwe sanatchulidwe.