Mawu a M'munsi
b Lemba la Miyambo 6:16 lili ndi chitsanzo cha mawu a Chiheberi omwe amatsindika kwambiri za nambala yachiwiri poisiyanitsa ndi nambala yoyamba. Kutchula zinthu m’njira imeneyi kumapezeka kawirikawiri m’Malemba.—Yobu 5:19; Miyambo 30:15, 18, 21.