Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pulofesa wina dzina lake Robert L. Thomas, analemba zokhudza nambala ya 144,000 imene imatchulidwa pa Chivumbulutso 7:4. Iye anati: “Nambala yotchulidwa palembali ndi ya chiwerengero chenicheni cha anthu mosiyana ndi anthu otchulidwa pa Chivumbulutso 7:9 omwe chiwerengero chawo sichikudziwika. Nambalayi ikanakhala kuti si chiwerengero chenicheni cha anthu, ndiye kuti manambala onse otchulidwa m’bukuli sakanakhalanso onena za ziwerengero zenizeni.”​—Chivumbulutso 1–7: Buku Exegetical Commentary, tsamba 474.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena