Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Mosiyana ndi zimene zili mu Tora, nthawi zambiri malamulo a miyambo ya Ayuda ankaletsa akazi kuphunzira Tora. Mwachitsanzo, mu Mishnah muli mawu a Rabbi Eliezer ben Hyrcanus yemwe anati: “Aliyense wophunzitsa mwana wake wamkazi Tora, zili ngati akumuphunzitsa zolaula.” (Sota 3:4) Mu Jerusalem Talmud muli chiganizo choti: “Kuli bwino kuti mawu a mu Tora awotchedwe ndi moto kusiyana n’kuti aphunzitsidwe kwa akazi.”—Sota 3:19a.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena