Mawu a M'munsi
a Ngati mwayamba kukhala ndi maganizo ofuna kudzipha, pemphani munthu wamkulu wodalirika kuti akuthandizeni mwamsanga. Kuti mudziwa zambiri, onani nkhani yokhala ndi mbali 4 ya mutu wakuti “Kodi Kudzipha Ndi Njira Yothetsera Mavuto?” mu Galamukani! ya April 2014.