Mawu a M'munsi
a Nkhaniyi ikufotokoza mavuto a kusinthasintha mmene munthu amamvera ndipo zimenezi zimachitikira achinyamata ambiri. Ngati muli ndi matenda ovutika maganizo a mtundu wina uliwonse, onani nkhani ya mutu wakuti “Kodi Ndingatani Ngati Ndili ndi Matenda Ovutika Maganizo?”