Mawu a M'munsi
a Dzina lakuti “Anefili” limachokera ku liwu la Chiheberi lomwe limatanthauza kuti “Ogwetsa.” Buku lina linanena kuti liwu limeneli limanena za anthu omwe “amagwera anthu ena mwachiwawa ndi kuwavulaza, ndipo amachititsa kuti enawo agwenso.”—Wilson’s Old Testament Word Studies.