Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Buku lina linafotokoza mmene anthu anayambira kusala kudya kwa masiku 40 pokonzekera isitala. Bukuli linati: “M’zaka za m’ma 300 C.E., anthu akamakonzekera phwando la pasika (Isitala) ankasala kudya kwa mlungu umodzi wokha, ndipo nthawi zinanso ankangosala kwa tsiku limodzi kapena awiri basi. Mawu onena za kusala kudya kwa masiku 40 amapezeka m’lamulo la nambala 5 lomwe linatuluka pamsonkhano wa akuluakulu achipembedzo wa ku Nicaea (mu 325 C.E) ngakhale kuti akatswiri ena amatsutsa zoti ankanena za kusala kudya kwa masiku 40 poyembekezera kuchita Isitala.”​—New Catholic Encyclopedia, Second Edition, Volume 8, patsamba 468.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena