Mawu a M'munsi
a Mawu akuti kusuta akutanthauza kupuma mwadala utsi wa fodya kaya kudzera m’ndudu kapena m’mapaipi. Ndipo mfundo za m’Baibulo zimagwiranso ntchito kwa anthu amene amachita kutafuna fodya, kununkhiza kapena kwa amene amagwiritsa ntchito mankhwala aliwonse osokoneza bongo..