Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Bungwe Loona za Akatswiri Osewera Tenesi ndi lomwe limayang’anira akatswiri a amuna osewera tenesi m’madera osiyanasiyana. Bungweli limakhala ndi m’ndandanda wa akatswiri komanso mipikisano yosiyanasiyana ndipo amapereka mphoto kwa owina potengera mapointi omwe apeza. Akawerengetsera mapointi omwe osewera apeza pa mipikisano yomwe inakhazikitsidwa, amasankha omwe akuyenera kuikidwa pam’ndandanda wa akatswiri a tenesi padziko lonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena