Mawu a M'munsi
a Mulungu ankagwiritsanso ntchito angelo ena akafuna kulankhula ndi anthu, osati Mawu yekha. Mwachitsanzo, Mulungu anagwiritsa ntchito angelo ena, osati Mwana wake Woyamba Kubadwa, popereka Chilamulo kwa Aisiraeli.—Machitidwe 7:53; Agalatiya 3:19; Aheberi 2:2, 3.