Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 151
  • Iye Adzaitana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Iye Adzaitana
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Iye Adzaitana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 151

NYIMBO 151

Iye Adzaitana

Losindikizidwa

(Yobu 14:​13-15)

  1. 1. Moyo wathu sumachedwa kutha,

    Timafadi mwamsanga.

    Mukanthawi kochepa kwambiri

    Timayamba kulira.

    Kodi akufa angadzauke?

    M’lungu akulonjeza:

    (KOLASI)

    Iye adzawaitana,

    Akufa adzayankha.

    Akulakalakatu

    Ntchito ya manja ake.

    Mulungu adzatidzutsa

    Chonde musakaike.

    Tidzakhala kosatha

    Mongadi anthu ake.

  2. 2. Anthu a M’lungu akamwalira

    Iye sawaiwala.

    Akuwakumbukira onsewo,

    Iye adzawadzutsa

    Ndipo tonsefe tidzakhaladi

    Ndi moyo mpaka kale.

    (KOLASI)

    Iye adzawaitana,

    Akufa adzayankha.

    Akulakalakatu

    Ntchito ya manja ake.

    Mulungu adzatidzutsa

    Chonde musakaike.

    Tidzakhala kosatha

    Mongadi anthu ake.

(Onaninso Yoh. 6:40; 11:​11, 43; Yak. 4:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena