Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 52
  • Kudzipereka Monga Mkhristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzipereka Monga Mkhristu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tidzipereke Monga Akhristu
    Imbirani Yehova
  • Kudzipatulira Kwachikristu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 52

NYIMBO 52

Kudzipereka Monga Mkhristu

Losindikizidwa

(Aheberi 10:​7, 9)

  1. 1. Yehova Mulungu wathu

    Analenga zonse.

    Dzikoli ndi mlengalenga

    Zonsezi ndi zake.

    Iye watipatsa moyo,

    Wasonyeza kuti

    Ndi woyenera kum’tamanda

    Ndiponso kum’lambira.

  2. 2. Yesu atabatizidwa

    Anauza M’lungu:

    ‘Ndabwera kuti ndichite

    Chifuniro chanu.’

    Mulungu anamudzoza

    Atabatizidwa

    Kuti azimutumikira

    Monga wodzipereka.

  3. 3. Yehova ife tabwera

    Kukutamandani.

    Tadzipereka kwa inu

    Ndipo tadzikana.

    Munatikonda kwambiri

    Potipatsa Yesu.

    Tasiya zomwe timafuna

    Tizichita za inu.

(Onaninso Mat 16:24; Maliko 8:​34; Luka 9:​23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena