Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 100
  • Alandireni Bwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Alandireni Bwino
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Alandireni Bwino
    Imbirani Yehova
  • ‘Cherezani Alendo’
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kuchereza Alendo Ndi Kofunika Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Tizichitira Ena “Zabwino” Pokhala Ochereza (Mat. 12:35a)
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 100

NYIMBO 100

Alandireni Bwino

Losindikizidwa

(Machitidwe 17:7)

  1. 1. Yehova ndi M’lungu wopanda tsankho.

    Amasamalira mosakondera.

    Amatipatsatu

    Kuwala ndi mvula,

    Amatipatsanso chakudya.

    Timatsanzira Yehova Mulungu

    Ngati tikuthandiza osauka.

    Adzatidalitsa

    Tikamasonyeza

    Anthu onse kukoma mtima.

  2. 2. Pothandiza ena sitingadziwe

    Madalitso omwe tingalandire.

    Ngakhale ndi oti

    Sitikuwadziwa,

    Tiwapatse zosowa zawo.

    Monga Lidiya wa m’nthawi yakale,

    Akabwera kwathu tiwalandire.

    M’lungu amaona

    Tikamutsanzira

    Pochitira anthu chifundo.

(Onaninso Mac. 16:​14, 15; Aroma 12:13; 1 Tim. 3:2; Aheb. 13:2; 1 Pet. 4:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena