Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chigawo 1
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 1

      Mulungu amalankhula nafe kudzera m’Baibulo. 2 Timoteyo 3:16

      Anthu kulikonse akumvetsera. Mateyu 28:19

  • Chigawo 2
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 2

      Yehova analenga chilichonse kumwamba . . . ndi padziko lapansi. Salimo 83:18; Chivumbulutso 4:11

  • Chigawo 3
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 3

      Yehova anapatsa Adamu ndi Hava zinthu zabwino zambiri. Genesis 1:28

      Mulungu anawauza kuti asadye chipatso cha mtengo umodzi. Genesis 2:16, 17

  • Chigawo 4
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 4

      Adamu ndi Hava sanamvere Mulungu, choncho anafa. Genesis 3:6, 23

      Akufa sadziwa chilichonse, amangokhala ngati fumbi. Genesis 3:19

  • Chigawo 5
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 5

      Anthu ambiri m’nthawi ya Nowa ankachita zoipa. Genesis 6:5

      Nowa anamvera Mulungu ndipo anapanga chingalawa. Genesis 6:13, 14, 18, 19, 22

  • Chigawo 6
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 6

      Mulungu anawononga anthu oipa, koma anapulumutsa Nowa ndi banja lake. Genesis 7:11, 12, 23

      Posachedwapa, Mulungu awononganso oipa ndi kupulumutsa anthu abwino. Mateyu 24:37-39

  • Chigawo 7
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 7

      Yehova anatumiza Yesu padziko lapansi. 1 Yohane 4:9

      Yesu ankachita zinthu zabwino koma anthu ankadana naye. 1 Petulo 2:21-24

  • Chigawo 8
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 8

      Yesu anatifera kuti tipeze moyo. Yohane 3:16

      Mulungu anaukitsa Yesu ndipo anamuika kukhala Mfumu ya Ufumu wa Mulungu. Danieli 7:13, 14

  • Chigawo 9
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 9

      Mavuto amene tikukumana nawo padziko lapansi akusonyeza kuti Ufumu wa Mulungu uli pafupi. Luka 21:10, 11; 2 Timoteyo 3:1-5

      Ufumuwo udzachotsa zoipa zonse. 2 Petulo 3:13

  • Chigawo 10
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 10

      Ambiri mwa anthu amene anamwalira adzaukitsidwa padziko lapansi. Machitidwe 24:15

      Ufumu wa Mulungu udzathetsa mavuto onse. Chivumbulutso 21:3, 4

  • Chigawo 11
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 11

      Mulungu amamvetsera mapemphero athu. 1 Petulo 3:12

      Tingatchule zinthu zosiyanasiyana popemphera. 1 Yohane 5:14

  • Chigawo 12
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 12

      Chikondi n’chofunika kwambiri kuti aliyense m’banja akhale wosangalala. Aefeso 5:33

      Khalani okoma mtima ndiponso okhulupirika, osati ankhanza. Akolose 3:5, 8-10

  • Chigawo 13
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 13

      Muzipewa kuchita zinthu zoipa. 1 Akorinto 6:9, 10

      Muzichita zinthu zabwino. Mateyu 7:12

  • Chigawo 14
    Mverani Mulungu
    • Chigawo 14

      Khalani kumbali ya Mulungu. 1 Petulo 5:6-9

      Sankhani mwanzeru, mverani Mulungu. Mateyu 7:24, 25

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena