Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rj tsamba 3
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Bwererani kwa Yehova
Bwererani kwa Yehova
rj tsamba 3

Zamkatimu

GAWO 1 N’CHIFUKWA CHIYANI MUYENERA KUBWERERA KWA YEHOVA?

Atumiki akale a Yehova ankakumana ndi mavuto ofanana ndi athu. Yehova ankawathandiza ndipo amalonjeza kuti adzatithandizanso masiku ano. Iye ali ngati M’busa wachikondi ndipo amafufuza anthu amene asochera n’kuwathandiza kuti abwerere.

Gawo 1 “Nkhosa Zosochera Ndidzazifunafuna”

GAWO 2 MPAKA 4 MAVUTO AMENE ANGAKULEPHERETSENI KUBWERERA KWA YEHOVA

Pali atumiki ena okhulupirika amene anafooka chifukwa cha nkhawa, kukhumudwa kapena kudziimba mlandu. Werengani kabukuka kuti muone mmene Yehova anawathandizira kuti ayambenso kumutumikira mosangalala.

Gawo 2 “Timapanikizidwa Mwamtundu Uliwonse”

Gawo 3 Tikakhala ndi “Chifukwa Chodandaulira”

Gawo 4 “Ndiyeretseni kuTchimo Langa”

Gawo 5 N’CHIYANI CHINGAKUTHANDIZENI KUBWERERA KWA YEHOVA?

Mu gawo 5 muli umboni wosonyeza kuti Yehova akufuna kuti mubwerere. Muonanso zimene Akhristu ena anachita kuti abwerere, mmene mpingo unawalandirira komanso mmene akulu anawathandizira.

Gawo 5 Bwererani kwa ‘M’busa Wanu ndi Woyang’anira Moyo Wanu’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena