Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb16 tsamba 80-tsamba 81 ndime 1
  • Indonesia

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Indonesia
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
yb16 tsamba 80-tsamba 81 ndime 1
Anthu awiri a Mboni za Yehova akulalikira mumsika ku Indonesia

Indonesia

WERENGANI nkhani yosangalatsa yonena za Akhristu odzichepetsa amene anakhalabe olimba mtima pa nthawi imene ankakumana ndi mavuto. Iwo anakumana ndi mavutowa chifukwa cha kusintha kwa zinthu pa nkhani zandale, mikangano ya zipembedzo, komanso kuletsedwa kwa ntchito yawo kwa zaka 25 kumene atsogoleri azipembedzo anachititsa. Mupezanso nkhani ya m’bale amene dzina lake linali pa gulu la anthu omwe ankayenera kuphedwa ndi chipani cha Chikomyunizimu. Mulinso nkhani ya munthu wina yemwe poyamba anali mtsogoleri wa gulu lina la zigawenga koma panopa ndi Mkhristu wodalirika. Muwerenganso nkhani yosangalatsa ya atsikana awiri omwe ali ndi vuto losamva, amene anayamba kugwirizana kwambiri koma kenako anazindikira kuti ndi pachibale. Mudziwanso mmene ntchito ya anthu a Yehova ikuyendera pamene akulalikira uthenga wabwino kwa anthu ambiri omwe ndi achisilamu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena