Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Moyo wa Makolo Akale
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • Makolo Akale M’Dziko Lolonjezedwa

      Dina mwana wa Yakobo atagwiriridwa ku Sekemu, Yakobo anasamuka kukakhala ku Beteli. Koma kodi mungayerekezere mtunda umene ana a Yakobo anafikako podyetsa nkhosa zake, kumene Yosefe anakawapeza? Mapu ali pano (ndi pamasamba 18-19) angakuthandizeni kuona mtunda umene unali pakati pa Beteli ndi Dotana. (Gen. 35:1-8; 37:12-17) Abale a Yosefe anam’gulitsa kwa amalonda amene anali kupita ku Igupto. Kodi mukuganiza kuti amalondawo, pa chochitika chimene chinachititsa kuti Aisrayeli asamukire ku Igupto ndi kudzachokako, anadutsa njira iti?—Gen. 37:25-28.

  • Moyo wa Makolo Akale
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • [Njira Zazikulu]

      Via Maris

      Msewu Wachifumu

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena