-
Moyo wa Makolo Akale‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
Dina mwana wa Yakobo atagwiriridwa ku Sekemu, Yakobo anasamuka kukakhala ku Beteli. Koma kodi mungayerekezere mtunda umene ana a Yakobo anafikako podyetsa nkhosa zake, kumene Yosefe anakawapeza? Mapu ali pano (ndi pamasamba 18-19) angakuthandizeni kuona mtunda umene unali pakati pa Beteli ndi Dotana. (Gen. 35:1-8; 37:12-17) Abale a Yosefe anam’gulitsa kwa amalonda amene anali kupita ku Igupto. Kodi mukuganiza kuti amalondawo, pa chochitika chimene chinachititsa kuti Aisrayeli asamukire ku Igupto ndi kudzachokako, anadutsa njira iti?—Gen. 37:25-28.
-
-
Moyo wa Makolo Akale‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
[Njira Zazikulu]
Via Maris
Msewu Wachifumu
-