Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Mumatsitsimula Ena?
    Nsanja ya Olonda—2007 | November 15
    • Kodi Mumatsitsimula Ena?

      CHAKUM’MWERA kwa mapiri a Lebanon kuli phiri la Hermoni lomwe ndi lalitali mamita 2,814. Nthawi zambiri pamwamba paphirili pamakutidwa ndi chipale chofewa. Ndipo zimenezi zimachititsa kuti kudzichita mame chifukwa cha mpweya wotentha umene umadutsa usiku. Mamewa amatsikira m’munsi mwa phirili mmene muli mitengo yosiyanasiyana ndiponso minda yampesa. Kalekale ku Isiraeli, m’nyengo ya chilimwe yomwe inkakhala yaitali, mame amenewa ankathandiza kuti kuzikhala chinyezi ndipo zomera zambiri zizisangalala.

      Nyimbo ina youziridwa ndi Mulungu, imayerekezera umodzi umene uli pakati pa anthu olambira Yehova ndi “mame a ku Hermoni, akutsikira pa mapiri a Ziyoni.” (Salmo 133:1, 3) Mofanana ndi phiri la Hermoni limene linkachititsa zomera kusangalala chifukwa cha mame, ifenso tingatsitsimule anthu amene timakumana nawo. Kodi tingachite motani zimenezi?

  • Kodi Mumatsitsimula Ena?
    Nsanja ya Olonda—2007 | November 15
    • [Zithunzi patsamba 16]

      Mame a m’phiri la Hermoni ankachititsa kuti zomera zizisangalala

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena