Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1991 | August 1
    • Bukhu la Miyambo liri ndi mavesi ambiri amene amaima paokha monga ndemanga zapadera za uphungu, koma Miyambo 27:23 ndimbali ya gulu la mavesi akuti: ‘Udziwitsitse zoweta zako ziri bwanji, Samalira magulu ako. Pakuti chuma sichiri chosatha; Kodi korona alipobe mpaka mibadwo mibadwo? Amatuta maudzu, msipu uoneka, Achera masamba a kumapiri. Ana a nkhosa akuveka, Atonde aombera munda; Mkaka wa mbuzi udzakukwanira kudya; Ndi a pa banja lako ndi adzakazi ako.’​—Miyambo 27:23-27.

  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1991 | August 1
    • Mbusa wogwira ntchito zolimba ndi wosamala adali ndi magwero odalirika a chithandizo​—Yehova. Motani? Eya, Mulungu amagaŵira nyengo ndi kuzungulira kwawo zimene mwamasiku onse zimatulukapo nsipu wokwanira kudyetsa nkhosa. (Salmo 145:16) Pamene nsipu uwuma ku malo akuchidikha chifukwa cha kusintha kwa nyengo, ungakhale wochuluka ku malo akumtunda, kumene mbusa watcheru angapititseko nyama zake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena