Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nzeru Zothandiza Munthu Kukhala ndi Thanzi Labwino
    Galamukani!—2011 | August
    • “Mtima wodekha ndiwo moyo wa munthu.”—MIYAMBO 14:30.

  • Nzeru Zothandiza Munthu Kukhala ndi Thanzi Labwino
    Galamukani!—2011 | August
    • Posiyanitsa munthu amene ali ndi mtima wodekha ndi amene sachedwa kupsa mtima, magazini ina ya zachipatala ya ku America (Journal of the American College of Cardiology), inati: “Kafukufuku waposachedwapa akusonyeza kuti anthu amene sachedwa kupsa mtima komanso amene amakonda kusunga mkwiyo, nthawi zambiri amadwala matenda a mtima.” Magaziniyo inapitiriza kuti: “Mankhwala abwino a matenda a mtima amaphatikizapo kupewa kupsa mtima ndi kusunga mkwiyo osati kungochita masewera olimbitsa thupi kapena kumwa mankhwala akuchipatala.” Mwachidule, tingati anthu amene ali ndi mtima wodekha amakhala ndi thanzi labwino, mogwirizana ndi zimene Baibulo limanena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena