Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • “Nzeru Itchinjiriza”
    Nsanja ya Olonda—2007 | July 15
    • Kodi kukhala ndi nzeru kumasintha bwanji zimene timalankhula? Mfumu yanzeruyi inati: “Wolabadira mawu adzapeza bwino; ndipo wokhulupirira Yehova adala. Wanzeru mtima adzatchedwa wochenjera; ndipo kukoma kwa milomo kuyenjezera kuphunzira. Nzeru ndi kasupe wa moyo kwa mwini wake; koma mwambo wa zitsiru ndi utsiru. Mtima wa wanzeru uchenjeza m’kamwa mwake, nuphunzitsanso milomo yake.”​—Miyambo 16:20-23.

  • “Nzeru Itchinjiriza”
    Nsanja ya Olonda—2007 | July 15
    • Motero n’zosabwitsa kuti “wanzeru mtima”amatchedwa wochenjera,”kapena kuti wozindikira. (Miyambo 16:21) Inde, nzeru yotereyi ndi “kasupe wa moyo” kwa anthu amene ali nayo. Nanga bwanji anthu opusa? Iwo ‘amanyoza nzeru ndi mwambo.’ (Miyambo 1:7) Kodi kusamvera chilango cha Yehova kumawabweretsera zotani? Amapitiriza kulangidwa, ndipo nthawi zambiri chilango chake chimakhala chachikulu kwambiri. Monga tanenera pamwambapa, Solomo anati: “Nzeru ndi kasupe wa moyo kwa mwini wake; koma mwambo wa zitsiru ndi utsiru.” (Miyambo 16:22) Anthu opusa angathenso kudziika m’mavuto, kudzichititsa manyazi, kudziputira matenda, ndiponso kufa msanga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena