Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nzeru Zothandiza Munthu Kukhala ndi Thanzi Labwino
    Galamukani!—2011 | August
    • “Mtima wosangalala ndiwo mankhwala ochiritsa.”—MIYAMBO 17:22.

  • Nzeru Zothandiza Munthu Kukhala ndi Thanzi Labwino
    Galamukani!—2011 | August
    • Komanso anthu omwe nthawi zambiri amakhala osangalala amapewa matenda a mtima. Dokotala wina wa ku Scotland, dzina lake Derek Cox, ananena pa wailesi ya BBC kuti: “Anthu amene amakhala osangalala, m’tsogolo sadzadwaladwala kuyerekeza ndi anthu amene sasangalala.” Iye ananenanso kuti: “Nthawi zambiri anthu amene amakhala osangalala sadwala matenda a mtima ndiponso ofa ziwalo.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena