-
“Adzadziŵa Kuti Ine Ndine Yehova”Nsanja ya Olonda—1988 | September 15
-
-
17. (a) Kodi ndi masomphenya otani amene Ezekieli anapatsidwa mu 593 B.C.E.? (b) Kukhalapo kwa kachisi wa m’masomphenya kuli umboni wa chiyani?
17 Mu 593 B.C.E., chaka cha 14 pambuyo pa kuwonongedwa kwa kachisi mu Yerusalemu, Ezekieli anapatsidwa masomphenya a malo opatulika atsopano a kulambira kwa Yehova. Oyesedwa ndi chitsogozo cha ungelo cha mneneriyo, anali a msinkhu waukulu koposa. (Ezekieli 40:1–48:35) Kachisi ameneyu anachitira chithunzi “hema wowona, amene Yehova anamuika,” ndipo anali ndi “zoimira za zinthu za kumwamba.” Yesu Kristu analowa m’Malo ake Opatulikitsa, “kumwamba kwenikweni,” mu 33 C.E. kukapereka kwa Mulungu mtengo wa nsembe yake ya dipo. (Ahebri 8:2; 9:23, 24) Kachisi wa masomphenya amatsimikizira kuti kulambira koyera kudzapulumuka kuukira kwa Gogi. Ndi chitonthozo chotani nanga kaamba ka okonda dzina la Yehova!
-
-
“Adzadziŵa Kuti Ine Ndine Yehova”Nsanja ya Olonda—1988 | September 15
-
-
[Mapu/Chithunzi patsamba 25]
(Onani m’magazini yeniyeni kuti mumvetse izi)
Chopereka chopatulika ndi ntchito ya mafuko
THE GREAT SEA
ENTERING IN TO HAMATH
DAN
ASHER
NAPHTALI
MANASSEH
EPHRAIM
REUBEN
JUDAH
THE CHIEFTAIN
Holy Contribution
En-Eglaim
BENJAMIN
SIMEON
En-gedi
ISSACHAR
ZEBULUN
Tamar
GAD
Meribath-Kadesh
Salt Sea
Jordan River
Sea of Galilee
-