Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • “Adzadziŵa Kuti Ine Ndine Yehova”
    Nsanja ya Olonda—1988 | September 15
    • 17. (a) Kodi ndi masomphenya otani amene Ezekieli anapatsidwa mu 593 B.C.E.? (b) Kukhalapo kwa kachisi wa m’masomphenya kuli umboni wa chiyani?

      17 Mu 593 B.C.E., chaka cha 14 pambuyo pa kuwonongedwa kwa kachisi mu Yerusalemu, Ezekieli anapatsidwa masomphenya a malo opatulika atsopano a kulambira kwa Yehova. Oyesedwa ndi chitsogozo cha ungelo cha mneneriyo, anali a msinkhu waukulu koposa. (Ezekieli 40:1–48:35) Kachisi ameneyu anachitira chithunzi “hema wowona, amene Yehova anamuika,” ndipo anali ndi “zoimira za zinthu za kumwamba.” Yesu Kristu analowa m’Malo ake Opatulikitsa, “kumwamba kwenikweni,” mu 33 C.E. kukapereka kwa Mulungu mtengo wa nsembe yake ya dipo. (Ahebri 8:2; 9:23, 24) Kachisi wa masomphenya amatsimikizira kuti kulambira koyera kudzapulumuka kuukira kwa Gogi. Ndi chitonthozo chotani nanga kaamba ka okonda dzina la Yehova!

  • “Adzadziŵa Kuti Ine Ndine Yehova”
    Nsanja ya Olonda—1988 | September 15
    • [Mapu/​Chithunzi patsamba 25]

      (Onani m’magazini yeniyeni kuti mumvetse izi)

      Chopereka chopatulika ndi ntchito ya mafuko

      THE GREAT SEA

      ENTERING IN TO HAMATH

      DAN

      ASHER

      NAPHTALI

      MANASSEH

      EPHRAIM

      REUBEN

      JUDAH

      THE CHIEFTAIN

      Holy Contribution

      En-Eglaim

      BENJAMIN

      SIMEON

      En-gedi

      ISSACHAR

      ZEBULUN

      Tamar

      GAD

      Meribath-Kadesh

      Salt Sea

      Jordan River

      Sea of Galilee

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena