Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mfundo Zazikulu za M’mabuku a Yoweli ndi Amosi
    Nsanja ya Olonda—2007 | October 1
    • 2:32​—Kodi ‘kuitana pa dzina la Yehova’ kumatanthauza chiyani? Kuitana pa dzina la Mulungu kumatanthauza kudziwa bwino dzinali, kulilemekeza kwambiri, ndiponso kudalira ndi kukhulupirira mwini wake wa dzinalo.​—Aroma 10:13, 14.

  • Mfundo Zazikulu za M’mabuku a Yoweli ndi Amosi
    Nsanja ya Olonda—2007 | October 1
    • 2:28-32. Anthu okhawo amene “adzaitana pa dzina la Yehova adzapulumutsidwa” pa “tsiku la Yehova lalikulu ndi loopsa.” Ndife oyamikira kuti Yehova amatsanulira mzimu wake pa anthu onse ndipo walola kuti ana ndi akulu omwe, amuna ndi akazi, agwire nawo ntchito yonenera, kapena kuti kulengeza “zinthu zazikulu za Mulungu.” (Machitidwe 2:11) Popeza tsiku la Yehova layandikira, tiyenera kukulitsa “khalidwe loyera” ndiponso kuchita ‘ntchito za kudzipereka kwa Mulungu.’​—2 Petulo 3:10-12.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena