Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsamba 2
  • ‘Yesetsani Kufunafuna Yehova Kuti Mupitirize Kukhala ndi Moyo’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Yesetsani Kufunafuna Yehova Kuti Mupitirize Kukhala ndi Moyo’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Mungapeze Chuma Chamtengo Woposa wa Golide!
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Kodi Mumafunsa Kuti, “Ali Kuti Yehova?”
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Funafunani Yehova, Amene Amayesa Mitima
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Mungapeze Thandizo
    Galamukani!—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 November tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AMOSI 1-9

“Yesetsani Kufunafuna Yehova Kuti Mupitirize Kukhala ndi Moyo”

5:6, 14, 15

Kodi kufunafuna Yehova kumatanthauza chiyani?

  • Kumatanthauza kupitiriza kuphunzira za iye komanso kutsatira mfundo zake pa moyo wathu

Kodi chinkachitika n’chiyani Aisiraeli akasiya kufunafuna Yehova?

  • Ankasiya ‘kudana ndi zoipa ndipo sankakonda zabwino’

  • Ankayamba kuchita zinthu zongodzisangalatsa okha

  • Ankasiya kutsatira malamulo a Yehova

    Mwisiraeli akudya komanso kumwa mwauchidakwa

Kodi Yehova watipatsa zinthu ziti pofuna kutithandiza kuti tizimufunafuna?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena