Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chipulumutso Nchothekera Pamene Mulungu Abwezera Chilango
    Nsanja ya Olonda—1989 | May 15
    • Yehova amamvetsera ku madandaulo a atumiki ake. Habakuku akufunsa kuti: “Yehova, ndidzafuula mpaka liti osamva inu?” Inde, palibe chilungamo, ndipo oipa azungulira olungama. Koma Mulungu amamva, ndipo monga gulu lake lopereka chilango, iye “awukitsa Akasidi.” Komabe, ndimotani mmene angagwiritsire ntchito mphamvu yonga nkhondo? Mneneriyo akuyembekezera yankho la Mulungu, akumadikira chidzudzulo.​—1:1–2:1.

  • Chipulumutso Nchothekera Pamene Mulungu Abwezera Chilango
    Nsanja ya Olonda—1989 | May 15
    • ○ 1:2-4​—Chikhulupiriro cha Habakuku mwa Yehova monga Mulungu yemwe samalekerera kuipa chinamufulumiza iye kufunsa chifukwa chimene kuipa kunafalikira. Iye anali wofunitsitsa kuti malingaliro ake awongoleredwe. (2:1) Pamene timadabwa chifukwa chimene zinthu zina zimalekereredwa, chidaliro chathu m’chilungamo cha Yehova chiyenera mofananamo kutithandiza kusunga kulinganizika kwathu ndi kuyembekeza pa iye.​—Salmo 42:5, 11.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena