Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chipulumutso Nchothekera Pamene Mulungu Abwezera Chilango
    Nsanja ya Olonda—1989 | May 15
    • Kokha olungama ndi okhulupirika adzakhalabe ndi moyo. Yehova akutsimikizira Habakuku za ichi. Ngakhale kuti pangawoneke kukhala kuchedwa, pa nthaŵi yoikidwiratu ya Mulungu masomphenya aulosi “afika ndithu, osazengereza.” Mdani wodzitukumulayo yemwe akulanda mitundu sadzachifikira chonulirapo chake. Ndithudi, Akasidiwo sadzapita osalangidwa.​—2:2-5.

  • Chipulumutso Nchothekera Pamene Mulungu Abwezera Chilango
    Nsanja ya Olonda—1989 | May 15
    • ○ 2:5​—Ababulo anali mwamuna wokhalamo ambiri amene anagwiritsira ntchito makina ake a nkhondo kugonjetsa mitundu. Mofanana ndi Shelo ndi imfa zimene nthaŵi zonse ziri zokonzekera kaamba ka minkhole yowonjezereka, iye anakhumba kugonjetsa kwa nkhondo kowonjezereka. (Yerekezani ndi Miyambo 30:15, 16.) Monga osonkhezeredwa ndi kumwa kwamphamvu, iye anakhala wopambana ndi zilakiko. Koma nkhondo zake za kugonjetsa zinatha pamene Babulo anagwa mu 539 B.C.E.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena