Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ambuye Wowona Adza Kaamba ka Chiweruzo
    Nsanja ya Olonda—1989 | July 1
    • Yehova samawona mopepuka awo osasonyeza ulemu kaamba ka kakonzedwe ka ukwati. Mosiyana ndi lamulo la Mulungu, amuna a ku Yuda adzitengera akazi achilendo. (Deuteronomo 7:3, 4) Iwo achita mwachinyengo ndi akazi a uchichepere wawo mwa kuwasudzula iwo. Yehova “adana nako kulekana,” Malaki akuchenjeza tero.​—2:10-17.

  • Ambuye Wowona Adza Kaamba ka Chiweruzo
    Nsanja ya Olonda—1989 | July 1
    • ○ 2:13​—Amuna ambiri a Chiyuda anali kusudzula akazi a uchichepere wawo, mwinamwake kuti akwatire akazi akunja achichepere. Guwa la Yehova linaphimbidwa ndi misozi​—mwachiwonekere ija ya akazi okanidwa omwe anabwera ku malo oyera kutsanula chisoni chawo pamaso pa Mulungu.​—Malaki 2:11, 14, 16.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena