Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ndinu Wofunika Kwambiri kwa Mulungu!
    Galamukani!—1999 | June 8
    • Mwachitsanzo, Yesu, pochitira fanizo kufunika kwa aliyense wa ophunzira ake, anati: “Kodi mpheta ziŵiri sizigulidwa kakhobiri? Ndipo imodzi ya izo siigwa pansi popanda Atate wanu [kudziŵa, NW]: komatu inu, matsitsi onse a m’mutu mwanu aŵerengedwa. Chifukwa chake musamawopa; inu mupambana mpheta zambiri.” (Mateyu 10:29-31) Taganizirani mmene mawu amenewo analimbikitsira omvetsera a Yesu a m’zaka za zana loyamba.

  • Ndinu Wofunika Kwambiri kwa Mulungu!
    Galamukani!—1999 | June 8
    • Kodi mukulimvetsetsa fanizo la Yesu lotonthoza mtimali? Ngati Yehova amaona kuti ngakhale timbalame ting’onoting’ono n’tofunika kwambiri kwa iye, nanga kuli bwanji ndi atumiki ake a padziko lapansi! Yehova amatizindikira ngakhale tili m’chigulu. Tonsefe Yehova amationa monga ofunika kwambiri kwa iye motero amayang’ana chilichonse cha ife—tsitsi lathu lenilenili, amaliŵerenga palokha palokha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena