Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsamba 3
  • Zimene Tikuphunzira pa Zomwe Yesu Anaphunzitsa pa Ulaliki Wapaphiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tikuphunzira pa Zomwe Yesu Anaphunzitsa pa Ulaliki Wapaphiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Chakudya pa Nthawi ya Njala
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • “Timakonda Kwambiri TV ya JW Broadcasting”
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
  • Kodi Mupitiriza Kutumikira Yehova Mosalekeza?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Mapulogalamu a pa JW Broadcasting ‘Ndi Othandiza Komanso Olimbikitsa Kwambiri’
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 January tsamba 3
Opemphapempha

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 4-5

Zimene Tikuphunzira pa Zomwe Yesu Anaphunzitsa pa Ulaliki Wapaphiri

5:3

Kodi mumazindikira zosowa zanu zauzimu?

Kamnyamata kosangalala

Mawu akuti “amene amazindikira zosowa zawo zauzimu” kwenikweni amatanthauza “anthu amene amapempha mzimu.” (Mat. 5:3) Tingasonyeze kuti tikufuna kuti Mulungu azititsogolera ndi mzimu wake ngati . . .

  • timawerenga Baibulo tsiku ndi tsiku

  • timakonzekera komanso kupezeka pamisonkhano

  • timawerenga mabuku athu, komanso ngati n’zotheka, zinthu zosiyanasiyana zopezeka pawebusaiti yathu

  • timaonera pulogalamu ya JW Broadcasting ya mwezi uliwonse

Kodi ndingatani kuti nthawi zonse ndizikonda kuphunzira Mawu a Mulungu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena