-
Fanizo la Anthu Ogwira Ntchito M’munda wa MpesaYesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
-
-
“Pakuti ufumu wakumwamba uli ngati mwinimunda wa mpesa, amene analawirira m’mawa kwambiri kukafuna anthu aganyu kuti akagwire ntchito m’munda wake wa mpesa. Aganyu amenewa atagwirizana nawo kuti aziwapatsa ndalama ya dinari imodzi pa tsiku, anawatumiza kumunda wake wa mpesa. Pafupifupi 9 koloko m’mawa anapitanso kukafuna anthu ena, ndipo anaona ena atangoimaima pamsika alibe chochita. Amenewonso anawauza kuti, ‘Inunso kagwireni ntchito m’munda wa mpesa. Ndidzakupatsani malipiro oyenerera.’ Chotero iwo anapita. Pafupifupi 12 koloko ndi 3 koloko masana, mwinimunda uja anapitanso kukachita chimodzimodzi. Pamapeto pake, pafupifupi 5 koloko madzulo anapitanso ndipo anakapeza ena atangoimaima. Iye anawafunsa kuti, ‘N’chifukwa chiyani mwangoimaima pano tsiku lonse osagwira ntchito?’ Iwo anamuyankha kuti, ‘Chifukwa palibe amene watilemba ganyu.’ Iye anawauza kuti, ‘Inunso pitani kumunda wanga wa mpesa.’”—Mateyu 20:1-7.
-
-
Fanizo la Anthu Ogwira Ntchito M’munda wa MpesaYesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
-
-
“Pakuti ufumu wakumwamba uli ngati mwinimunda wa mpesa, amene analawirira m’mawa kwambiri kukafuna anthu aganyu kuti akagwire ntchito m’munda wake wa mpesa. Aganyu amenewa atagwirizana nawo kuti aziwapatsa ndalama ya dinari imodzi pa tsiku, anawatumiza kumunda wake wa mpesa. Pafupifupi 9 koloko m’mawa anapitanso kukafuna anthu ena, ndipo anaona ena atangoimaima pamsika alibe chochita. Amenewonso anawauza kuti, ‘Inunso kagwireni ntchito m’munda wa mpesa. Ndidzakupatsani malipiro oyenerera.’ Chotero iwo anapita. Pafupifupi 12 koloko ndi 3 koloko masana, mwinimunda uja anapitanso kukachita chimodzimodzi. Pamapeto pake, pafupifupi 5 koloko madzulo anapitanso ndipo anakapeza ena atangoimaima. Iye anawafunsa kuti, ‘N’chifukwa chiyani mwangoimaima pano tsiku lonse osagwira ntchito?’ Iwo anamuyankha kuti, ‘Chifukwa palibe amene watilemba ganyu.’ Iye anawauza kuti, ‘Inunso pitani kumunda wanga wa mpesa.’”—Mateyu 20:1-7.
-
-
Fanizo la Anthu Ogwira Ntchito M’munda wa MpesaYesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
-
-
Zikuoneka kuti atsogoleri achipembedzo, mwachitsanzo Afarisi amene anayesa Yesu pomufunsa nkhani zokhudza kuthetsa banja, anali ngati akhala akugwira ntchito mwakhama potumikira Mulungu. Anali ngati anthu amene ankagwira ntchito nthawi zonse ndipo ankayembekezera kulandira malipiro onse ndipo malipiro ake anali dinari imodzi, yomwe inali malipiro a tsiku limodzi.
-