-
Kodi Nkhosazo ndi Mbuzizo Zili ndi Mtsogolo Motani?Nsanja ya Olonda—1995 | October 15
-
-
3. Poyambirira m’nkhani yake, kodi Yesu anati nchiyani chidzachitika chitangoyamba chisautso chachikulu?
3 Yesu ananeneratu za zochitika zodabwitsa zimene zidzachitika “pomwepo” chitaulika chisautso chachikulu, zochitika zomwe tikuziyembekezera. Anati pomwepo padzaoneka “chizindikiro cha Mwana wa munthu.” Chimenechi chidzakhudza kwambiri “mitundu yonse ya pa dziko lapansi” imene “idzapenya Mwana wa munthu alinkudza pa mitambo ya kumwamba, ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu.” Mwana wa munthu adzatsagana ndi “angelo ake.” (Mateyu 24:21, 29-31)a Bwanji nanga za fanizo la nkhosa ndi mbuzi? Mabaibulo amakono amaliika m’chaputala 25, koma lili mbali ya yankho la Yesu, lomafotokoza zowonjezera ponena za kudza kwake ndi ulemerero ndipo lomasumika pa kuweruza kwake “mitundu yonse.”—Mateyu 25:32.
-
-
Kodi Nkhosazo ndi Mbuzizo Zili ndi Mtsogolo Motani?Nsanja ya Olonda—1995 | October 15
-
-
ONANI MBALI ZOFANANA
Mateyu 24:29-31 Mateyu 25:31-33
Chitayamba chisautso chachikulu, Mwana wa munthu afika
-