Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Anamwali Anzeru ndi Opusa
    Nsanja ya Olonda—1990 | April 15
    • M’fanizolo, anamwali khumiwo akupita ndi cholinga chokalandira mkwati ndi kugwirizana ndi operekeza ukwati. Pamene iye afika, iwo adzawunikira njira yopitamo aukwati ndi nyali zawo, mwakutero kumlemekeza pamene akubweretsa mkwatibwi wake ku nyumba yokonzedwera iye. Komabe, Yesu akulongosola kuti: “Opusawo, m’mene anatenga nyali zawo, sanadzitengeranso mafuta; koma anzeruwo anatenga mafuta m’nsupa zawo, pamodzi ndi nyali zawo. Ndipo pamene mkwati anachedwa, onsewo anaodzera, nagona tulo.”

  • Anamwali Anzeru ndi Opusa
    Nsanja ya Olonda—1990 | April 15
    • Mafutawo akuphiphiritsira chija chimene chimakhalitsa Akristu owona kuwala monga zowunikira, ndicho, Mawu ouziridwa a Mulungu, pa amene akugwira mwamphamvu, pamodzi ndi mzimu woyera, umene umawathandiza kumvetsetsa Mawuwo. Mafuta auzimu amakhozetsa kagulu ka anamwali ochenjera kuunikira polandira mkwati pamene akupita ku phwando la ukwati. Koma gulu la anamwali opusa alibe mwa iwo, m’nsupa zawo, mafuta auzimu ofunikira. Chotero Yesu akulongosola zimene zikuchitika:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena