Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1991 | May 15
    • Komabe, zinthu zina zimene Yesu ananena zinaposa pa maulendo olalikira a atumwi. Iye anaŵauza kuti: ‘Chenjerani ndi anthu; . . . adzamuka nanu kwa akazembe ndi mafumu chifukwa cha ine, kukhala mboni ya kwa iwo, ndi kwa anthu akunja.’ (Mateyu 10:17, 18) Paulendowo, atumwi 12 amenewo mwachiwonekere anakumana ndi chitsutso, koma palibe umboni wakuti iwo anatengedwa “kwa akazembe ndi mafumu” kukachitira umboni kwa “anthu akunja.”a M’zaka zapambuyo pake, atumwiwo anawonekera pamaso pa olamulira, onga Mfumu Herode Agripa I ndi II, Sergio Paulo, Galiyo, ndipo ngakhale Wolamulira Nero. (Machitidwe 12:1, 2; 13:6, 7; 18:12; 25:8-12, 21; 26:1-3) Chotero mawu a Yesu anagwira ntchito pambuyo pake.

  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1991 | May 15
    • a Matembenuzidwe ena amamasulira mawuwo “osapembedza” (The Jerusalem Bible), “Akunja” (New International Version ndi matembenuzidwe a Moffatt ndi Lamsa), ndi “osakhulupirira” (The New English Bible).

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena